security

25-Apr-2021 | 08:58

There is a lot of robbery in our community of baka Karonga and we need security step up from police

Kuchuluka kwa ngozi zanjinga

06-Dec-2019 | 11:25

Kuno ku Kasungu boma, ngozi zanjinga zikuchuluka. China mwazifukwa ndi kusasamala pa kayendedwe ka pansewu. Chonde a polisi tithandizeni.

robbery

10-Dec-2019 | 09:14

Ntonya near Christ citadel church

MAIZE SCARCITY AT BALAKA ADMARC

10-Dec-2019 | 09:23

There is inadequate supply of maize at the aforementioned satellite effective October 2019

kusowa kwa alangizi

10-Dec-2019 | 10:30

inadequate of extension workers here in Balaka

Chithandizo Kwa Anthu Omwe Nyumba Zinagwa

09-Jan-2020 | 06:36

Kuno kwa mgona pali anthu ena omwe nyumba zawo zinakokoloka ndi madzi, ena chithandizo analandira pomwe ena sanalandire

Njala ku Balaka

21-Jan-2020 | 11:14

Njala yafika povuta ku balaka makamaka dela la Mfumu yaikulu Phimbi pomwe anthu anayi sabata yatha anakomoka ndi njala zomwe zapangitsa phungu wa delali Ireen Mambala kugawa chakudya kwa ena mu delali

Kusowa Chilungamo pakagawidwe ka Chimanga

14-Jan-2020 | 10:31

Kuno ku Balaka Central East kagawidwe ka chimanga sikakuyenda bwino, ma khansala and akulu akulu azipani kumadera akumangoba thandizolo likabwera

Mutiunikire Za Malata Subsidy

05-Feb-2020 | 08:16

Kasungu West kwa Sub-TA Mawawa, kodi boma bwanji likupereka zithu zochepa pazipangizo zomwe adalonjeza? Ndalama ya labor K50,000 sakutipatsa, ma door frame ndi mawindow sakutipatsa. kodi nanga ngongoleyi tizabweza bwanji ngati katundu wina sititenga